MOYO WATHU WACHIKHRISTU Muzithandiza Anthu Osapembedza Kudziwa Mlengi Wawo YAMBANI Muzithandiza Anthu Osapembedza Kudziwa Mlengi Wawo Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu Kodi mumalephera kulalikira anthu osapembedza poganiza kuti mwina samvetsera uthenga wanu? Ngati ndi choncho, muzikumbukira kuti anthu ambiri amene sanali m’chipembedzo chilichonse, kuphatikizapo amene ankati kulibe Mulungu, anakhala a Mboni za Yehova. Nthawi zambiri anthu amenewa amangofunika kuwathandiza kupeza umboni woti kuli Mulungu.—Aro 1:20; 10:14. ONERANI VIDIYO YAKUTI ANTHU OPANDA CHIKHULUPIRIRO AKHOZA KUSINTHA N’KUKHALA NDI CHIKHULUPIRIRO—ANTHU OSAPEMBEDZA, KENAKO YANKHANI FUNSO LOTSATIRALI: Kodi zomwe zinachitikira Tommaso zakuthandizani bwanji kukhala ndi maganizo oyenera kuti muzilalikira kwa anthu osapembedza? Yankho Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena Muzithandiza Anthu Osapembedza Kudziwa Mlengi Wawo UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU–NDANDANDA YA MISONKHANO Muzithandiza Anthu Osapembedza Kudziwa Mlengi Wawo Chinenero Chamanja cha ku Malawi Muzithandiza Anthu Osapembedza Kudziwa Mlengi Wawo https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/202023341/univ/art/202023341_univ_sqr_xl.jpg mwb23.9 22