Kodi Dzikoli Latsala Pang’ono Kutha? YAMBANI Kodi Dzikoli Latsala Pang’ono Kutha? Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu Ngakhale kuti maulendo angapo anthu akhala akunena tsiku lenileni lomwe dzikoli lidzathe koma zomwe ankaganizazo sizinachitike. Ndiye kodi dzikoli lidzathadi? KODI BAIBULO LIMANENA ZOTANI? Kodi mapeto a dzikoli adzakhala otani? Kodi dzikoli lidzatha liti? Kodi mudzapulumuka? Kodi zinthu zidzakhala bwanji dzikoli likadzatha? Mungadabwe ndi mmene Baibulo likuyankhira mafunsowa m’magaziniyi ndipo mayankho ake akulimbikitsani kwambiri. A Mboni za Yehova adzasangalala kukuthandizani kudziwa zambiri zokhudza cholinga cha Mulungu. Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena Kodi Dzikoli Latsala Pang’ono Kutha? NSANJA YA OLONDA Kodi Dzikoli Latsala Pang’ono Kutha? Chinenero Chamanja cha ku Malawi Kodi Dzikoli Latsala Pang’ono Kutha? https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/2021088/univ/art/2021088_univ_sqr_xl.jpg wp21.2 8