Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda ndi Galamukani! a 2021
Wosonyeza deti la magazini imene muli nkhaniyo
NSANJA YA OLONDA YOPHUNZIRA
BAIBULO
Kodi zolemba pamwala zimene zapezeka zikugwirizana bwanji ndi Baibulo? Jan.
MAFUNSO OCHOKERA KWA OWERENGA
Kodi a Mboni ayenera kugwiritsa ntchito ma webusaiti othandiza kupeza wokwatirana naye? July
Kodi Paulo ankatanthauza chiyani pamene ananena kuti: “Mwa chilamulo, ine ndinafa ku chilamulo”? (Agal. 2:19), June
N’chifukwa chiyani tiyenera kusamala tikamagwiritsa ntchito mapulogalamu otumizira ndi kulandirira mauthenga? Mar.
N’chifukwa chiyani Yesu atatsala pang’ono kufa analankhula mawu a Davide a pa Salimo 22:1? Apr.
Tanthauzo la lamulo lakuti “usachite kanthu kalikonse kuti uphetse mnzako” (Lev. 19:16), Dec.
MBIRI YA MOYO WANGA
Ndakhala Ndikusangalala Kutumikira Yehova (J. Kikot), July
“Ndaphunzira Zambiri Kuchokera kwa Ena” (L. Breine), May
Ndimadalira Yehova Posankha Zochita (D. Yazbek), June
Ndinkafuna Moyo Watanthauzo (M. Witholt), Nov.
“Panopa Ndimakonda Kwambiri Utumiki” (V. Vicini), Apr.
Tinaphunzira Kuti Tisamakane Yehova Akatipatsa Zochita (K. Logan), Jan.
Yehova Wakhala ‘Akuwongola Njira Zanga’ (S. Hardy), Feb.
MBONI ZA YEHOVA
1921—Zomwe Zinachitika Zaka 100 Zapitazo, Oct.
MOYO NDI MAKHALIDWE ACHIKHRISTU
NKHANI ZOPHUNZIRA
Aliyense Mumpingo Angathandize Ophunzira Baibulo Kuti Abatizidwe, Mar.
Amene Mwangokwatirana Kumene, Muziika Kutumikira Yehova Pamalo Oyamba, Nov.
Buku la Levitiko Limatiphunzitsa Mmene Tingachitire Zinthu ndi Ena, Dec.
Chikondi Chimatithandiza Kupirira Ena Akamadana Nafe, Mar.
Khamu Lalikulu la Nkhosa Zina Likutamanda Mulungu ndi Khristu, Jan.
Kodi Achinyamata Mungatani Kuti Anthu Ena Azikudalirani? Mar.
Kodi Chikhulupiriro Chanu Chidzakhala Cholimba? Nov.
Kodi Kulapa Kwenikweni N’kutani? Oct.
Kodi Mudzakhumudwa N’kusiya Kutsatira Yesu? May
Kodi Mudzayembekezera Yehova Moleza Mtima? Aug.
Kodi Mungagwire Nawo Ntchito Yothandiza Anthu Kukhala Ophunzira a Yesu? July
Kodi Timapindula Bwanji ndi Chikondi Chokhulupirika cha Yehova? Nov.
Kodi Tingatani Kuti ‘Tilawe’ Ubwino wa Yehova? Aug.
Kodi Yehova Amatiteteza Bwanji? Mar.
Malemba Angatithandize Kuti Tizipirira, Mar.
“Mukhale Oyera,” Dec.
Mungathe Kupulumuka ku Misampha ya Satana, June
Munthu Amene Mumamukonda Akasiya Kutumikira Yehova, Sept.
Musafooke, Oct.
Musakhumudwitse “Tianati,” June
Musamakayikire Kuti Munapeza Choonadi, Oct.
Musamatekeseke Ndipo Muzidalira Yehova, Jan.
“Mutu wa Mkazi Ndi Mwamuna,” Feb.
“Mutu wa Mwamuna Aliyense Ndi Khristu,” Feb.
Muzikhulupirira Kwambiri Mlengi, Aug.
Muzikonda Kwambiri Yehova Komanso Abale ndi Alongo Anu, Sept.
Muzimvera Mawu a M’busa Wabwino, Dec.
Muziona Kuti Achikulire Okhulupirika Ndi Amtengo Wapatali, Sept.
Muziona Kuti Achinyamata Ndi Amtengo Wapatali, Sept.
Muzipewa Kuyambitsa Mpikisano Koma Muzilimbikitsa Mtendere, July
Muzisangalala ndi Utumiki Wanu, Aug.
Muzisangalala ndi Zimene Mukuchita Potumikira Yehova, July
Muzithandiza Ophunzira Baibulo Kuti Abatizidwe, June
Muzitsanzira Yehova pa Nkhani ya Kupirira, July
“Muzitsatira Mapazi Ake Mosamala Kwambiri,” Apr.
Muziyamikira Mwayi Wanu Wokhala M’banja la Yehova, Aug.
“Ndidzagwedeza Mitundu Yonse ya Anthu,” Sept.
Okonda Chilungamo Palibe Chowakhumudwitsa, May
Pitirizani ‘Kumumvera,’ Dec.
Pitirizani Kuona Utumiki Wanu Moyenera, May
Pitirizani Kusonyezana Chikondi Chenicheni, Jan.
Pitirizani Kusonyezana Chikondi Chokhulupirika, Nov.
Timatumikira Mulungu “Wachifundo Chochuluka,” Oct.
Tiziyamikira Mphatso ya Dipo, Apr.
Udindo Umene Akulu Ali Nawo Mumpingo, Feb.
Yehova Ali Nanu, Simuli Nokha, June
Yehova Amakuonani Kuti Ndinu Amtengo Wapatali, Apr.
Yehova Amatipatsa Mphamvu, May
Zimene Tingachite Kuti Tizisangalalabe Tikakumana ndi Mayesero, Feb.
Zimene Tingaphunzire Kwa “Wophunzira Amene Yesu Anali Kumukonda Kwambiri,” Jan.
Zimene Tingaphunzire pa Mawu Omaliza a Yesu, Apr.
NKHANI ZOSIYANASIYANA
NSANJA YA OLONDA YOGAWIRA