Zimene Zachitika M’chaka Chapitachi
Yehova anaonetsa Ezekieli masomphenya a galeta lalikulu lakumwamba. Galeta limeneli likuimira mbali yosaoneka ya gulu la Yehova. Ngakhale kuti galetali ndi lalikulu kwambiri, likuthamanga pa liwiro lalikulu ndipo likutha kukhotera kwina kulikonse mofulumira kwambiri. (Ezek. 1:15-28) Zinthu zosangalatsa zimene zachitika m’chaka chapitachi zikusonyeza kuti mbali yapadziko lapansi ya gulu la Yehova Mulungu ilinso pa liwiro lalikulu.
M'CHIGAWO ICHI
Gulu la Yehova Likupita Patsogolo
Mmene ntchito yosamutsa likulu lathu kuchoka ku New York City ikuyendera, zikusonyezeratu kuti Yehova akutitsogolera.
WEBUSAITI YA JW.ORG—Ikuchitira “Umboni ku Mitundu Yonse”
Webusaiti yathu ikuthandiza kuti anthu a “mitundu yonse” amve uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu.”
Akusangalala ndi LAIBULALE YA PA INTANETI ya Watchtower
Anthu amene akugwiritsa ntchito laibulale imeneyi anatitumizira makalata oyamikira.
Ana Akusangalala ndi Mavidiyo a Makatuni
Werengani nkhaniyi kuti muone mmene mavidiyowa akuthandizira ana ndiponso mabanja padziko lonse.
Chionetsero Chosangalatsa cha Mbiri ya Mboni za Yehova
Werengani nkhaniyi kuti mumve za chionetsero chatsopano cha mbiri ya Mboni za Yehova komanso zina zimene zachitikira Akhristu.
Lipoti la Milandu
Malipoti a milandu yochokera m’mayiko 12 amenewa akusonyeza kuti mayiko ambiri akupha ufulu wolambira wa Mboni za Yehova.
Malipoti Apadera—Zochitika M’mayiko Osiyanasiyana
A Mboni za Yehova akuyesetsa kumanga malo abwino olambirira Mulungu.
Mwambo Wopereka Nthambi
Onani zinthu zina zosangalatsa zimene zinachitika pa mwambowu m’mayikowo