Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Kuona Malo ku Beteli

Tikukuitanani kuti mudzaone maofesi athu a nthambi omwenso amadziwika kuti Beteli. Ku maofesi athu ena kulinso malo achionetsero omwe mukhoza kuona nokha popanda wokutsogolerani.

Kuyambiranso Kuona Malo: M'mayiko ambiri, anthu adzayambiranso kuona malo m'maofesi athu a nthambi kuyambira pa 1 June, 2023. Kuti mudziwe zambiri, lankhulani ndi abale a ku nthambi yomwe mukufuna kukaonayo. Komabe, musapite kukaona malo ngati mwapezeka ndi COVID-19 kapena ngati muli ndi zizindikiro za chimfine kapenanso ngati posachedwapa munakumana ndi munthu amene wapezeka ndi COVID-19.

Benin

ARTJB (Association religieuse des Témoins de Jéhovah du Bénin)

Route Inter-Etat Cotonou-Parakou

AB-CALAVI

BENIN

+229 97-97-95-33

+229 97-97-95-34

+229 21-36-04-57 (Fax)

Kuona Malo

Lolemba mpaka Lachisanu

8:00 a.m. mpaka 10:45 a.m. ndi 1:00 p.m. mpaka 3:45 p.m.

Nthawi yonse: Mphindi 45

Zimene Timachita

Timamasulira mabuku a nkhani za m’Baibulo m’Chibariba, Chifoni, Chigani, Chijula, Chikabiye, Chimore ndi Chizama. Timatumiza mabuku kumagulu ndi ku mipingo yoposa 500, ku Benin, Burkina Faso, Niger, ndi Togo.

Koperani pepala losonyeza ofesi yathu.