Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Kuona Malo ku Beteli

Tikukuitanani kuti mudzaone maofesi athu a nthambi omwenso amadziwika kuti Beteli. Ku maofesi athu ena kulinso malo achionetsero omwe mukhoza kuona nokha popanda wokutsogolerani.

Kuyambiranso Kuona Malo: M'mayiko ambiri, anthu adzayambiranso kuona malo m'maofesi athu a nthambi kuyambira pa 1 June, 2023. Kuti mudziwe zambiri, lankhulani ndi abale a ku nthambi yomwe mukufuna kukaonayo. Komabe, musapite kukaona malo ngati mwapezeka ndi COVID-19 kapena ngati muli ndi zizindikiro za chimfine kapenanso ngati posachedwapa munakumana ndi munthu amene wapezeka ndi COVID-19.

Chile

Ave Concha y Toro 3456

PUENTE ALTO

CHILE

+56 2-428-2600

+56 2-428-2609 (Fax)

Kuona Malo

Lolemba mpaka Lachisanu

8:30 a.m., 9:30 a.m., 10:30 a.m., 1:30 p.m., 2:30 p.m., 3:30 p.m.

Nthawi yonse: Ola limodzi

Zimene Timachita

Timayang’anira ntchito yophunzitsa anthu Baibulo imene Mboni za Yehova zikugwira ku Chile. Timatumiza mabuku kumipingo yoposa 800.

Koperani pepala losonyeza ofesi yathu.