Onani zimene zilipo

Kukaona Malo pa Beteli

Tikuitanani kuti mudzaone maofesi athu a nthambi, amene timayacha kuti Beteli. Maofesi ena a nthambi ali na ma miziyamu yakuti munthu akhoza kudzionela yekha zinthu popanda wina kumutsogolela.

Kuyambilanso Kukayendela Maofesi a Nthambi: Pa June 1, 2023, m'maiko ambili tinayambilanso kulola anthu kukayendela maofesi athu a nthambi. Kuti mumve zambili, funsilani ku ofesi ya nthambi imene mufuna kukayendela. Koma conde, osapitako ngati munapezeka na COVID-19, ngati muli na cimfine, kapena ngati caposacedwa munakhalako pafupi na munthu wodwala COVID-19.

Chile

Ave Concha y Toro 3456

PUENTE ALTO

CHILE

+56 2-428-2600

+56 2-428-2609 (Fax)

Kuona Malo

Pa Mande mpaka pa Cisanu

9:00hrs mpaka 10:30hrs ndi 13:30hrs mpaka 15:00hrs

Nthawi yoona malo: Ola limodzi

Zimene Timacita

Timayang’anila nchito ya Mboni za Yehova yophunzitsa anthu Baibulo m’dzikoli. Timatumiza mabuku kumipingo yoposa 800.

Tengani kapepala koonetsa malo.