Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Kuona Malo ku Beteli

Tikukuitanani kuti mudzaone maofesi athu a nthambi omwenso amadziwika kuti Beteli. Ku maofesi athu ena kulinso malo achionetsero omwe mukhoza kuona nokha popanda wokutsogolerani.

Kuyambiranso Kuona Malo: M'mayiko ambiri, anthu adzayambiranso kuona malo m'maofesi athu a nthambi kuyambira pa 1 June, 2023. Kuti mudziwe zambiri, lankhulani ndi abale a ku nthambi yomwe mukufuna kukaonayo. Komabe, musapite kukaona malo ngati mwapezeka ndi COVID-19 kapena ngati muli ndi zizindikiro za chimfine kapenanso ngati posachedwapa munakumana ndi munthu amene wapezeka ndi COVID-19.

Malawi

Alendo Ndiponso Kuona Malo

Pemphani Kudzaona Malo

Onani Kapena Kusintha Zomwe Munapempha

Koperani pepala losonyeza ofesi yathu.

Zimene Timachita

Timamasulira mabuku ofotokoza nkhani za m’Baibulo m’Chichewa, Chitonga, Chitumbuka, Chiyao ndiponso Chinenero Chamanja cha ku Malawi. Timayang’aniranso ntchito imene mipingo ya Mboni za Yehova ikugwira m’Malawi.

Adiresi ndi Nambala za foni

Malo amene tikupezeka