Kukaona Malo pa Beteli
Tikuitanani kuti mudzaone maofesi athu a nthambi, amene timayacha kuti Beteli. Maofesi ena a nthambi ali na ma miziyamu yakuti munthu akhoza kudzionela yekha zinthu popanda wina kumutsogolela.
Kuyambilanso Kukayendela Maofesi a Nthambi: Pa June 1, 2023, m'maiko ambili tinayambilanso kulola anthu kukayendela maofesi athu a nthambi. Kuti mumve zambili, funsilani ku ofesi ya nthambi imene mufuna kukayendela. Koma conde, osapitako ngati munapezeka na COVID-19, ngati muli na cimfine, kapena ngati caposacedwa munakhalako pafupi na munthu wodwala COVID-19.
Zimbabwe
Plot 14 of Good Hope
Beema Road
Mount Hampden
HARARE
ZIMBABWE
+263 4-2910591
+263 712-604892
+263 772-472403
+263 772-472404
Kuona Malo
Pa Mande mpaka pa Cisanu
8:00hrs mpaka 11:00hrs ndi 13:00hrs mpaka 16:00hrs.
Nthawi yoona malo: Ola limodzi ndi hafu
Zimene Timacita
Ofesi ya ku Zimbabwe imayang’anila nchito ya Mboni za Yehova zoposa 39,000 m’dzikolo. Pa ofesiyi amamasulilanso mabuku ofotokoza Baibulo m’zinenelo zambili kuphatikizapo Cishona, Cindebele, ndi cinenelo ca manja ca ku Zimbabwe.