Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Zoti Muchite Pophunzira Baibulo

Munthu Wakhate Anachiritsidwa

Werengani nkhani ya m’Baibulo yonena za mmene kamtsikana ka ku Isiraeli kanathandizira mkulu wa asilikali a nkhondo wa ku Siriya kuti achiritsidwe. Koperani nkhani ya m’Baibuloyi, iwerengeni, ndipo muiganizire mozama n’kuona mmene ingakuthandizireni.