ZITHUNZI ZOFOTOKOZA NKHANI ZA M’BAIBULO
Mulungu Anatuma Mose ku Iguputo
Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene Yehova Mulungu anachita posonyeza kuti ndi wamphamvu kuposa Farao wa ku Iguputo amene anali wouma mtima. Mukhoza kuwerenga nkhaniyi pawebusaitiyi kapena patsamba limene mwasindikiza.