Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

ZITHUNZI ZOFOTOKOZA NKHANI ZA M’BAIBULO

Mulungu Anatuma Mose ku Iguputo

Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene Yehova Mulungu anachita posonyeza kuti ndi wamphamvu kuposa Farao wa ku Iguputo amene anali wouma mtima. Mukhoza kuwerenga nkhaniyi pawebusaitiyi kapena patsamba limene mwasindikiza.