ZITHUNZI ZOFOTOKOZA NKHANI ZA M’BAIBULO
Adamu ndi Hava Anachita Zinthu Modzikonda
Werengani nkhaniyi kuti mudziwe za Adamu ndi Hava omwe anasankha zinthu modzikonda ndipo zinachititsa kuti anthu onse azikumana ndi mavuto. Werengani nkhaniyi pawebusaiti yathu kapena patsamba limene mwasindikiza.