Phunziro 25: Mmene Mungapezere Anzanu
Anzanu enieni akhoza kukhala amsinkhu uliwonse ngati amakonda Yehova. Kodi anzanu ndi ndani?
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
ZOCHITA PA GAWO LA KHALANI BWENZI LA YEHOVA
Pezani Anzanu Enieni
N’chifukwa chiyani ndi bwino kukhala ndi anzanu omwe ndi achikulire?
MAVIDIYO
Phunzirani kwa Anzake a Yehova
Phunzirani zambiri kuchokera kwa anthu otchulidwa m’Baibulo omwe anakhala mabwenzi a Yehova!
ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA
Zoti Ana Achite
Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.