Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Phunziro 25: Mmene Mungapezere Anzanu

Phunziro 25: Mmene Mungapezere Anzanu

Anzanu enieni akhoza kukhala amsinkhu uliwonse ngati amakonda Yehova. Kodi anzanu ndi ndani?

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

ZOCHITA PA GAWO LA KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Pezani Anzanu Enieni

N’chifukwa chiyani ndi bwino kukhala ndi anzanu omwe ndi achikulire?

MAVIDIYO

Phunzirani kwa Anzake a Yehova

Phunzirani zambiri kuchokera kwa anthu otchulidwa m’Baibulo omwe anakhala mabwenzi a Yehova!

ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

Zoti Ana Achite

Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.