Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Ndakonzekera Kuchita Zambiri

Ndakonzekera Kuchita Zambiri

Tikakhala ndi zolinga zauzimu Yehova amaona kuti timaganizira kwambiri za iyeyo. Kodi iweyo uli ndi zolinga zotani?

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

Khalani Bwenzi la Yehova (nyimbo zina)

Ndakonzekera Kuchita Zambiri

Kodi zolinga zako zauzimu ndi zotani?

ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

Zoti Ana Achite

Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.