Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

JANUARY 16, 2014
ARMENIA

Dziko la Armenia Latulutsa M’ndende Anthu Amene Anamangidwa Chifukwa Chokana Kulowa Usilikali

Dziko la Armenia Latulutsa M’ndende Anthu Amene Anamangidwa Chifukwa Chokana Kulowa Usilikali

Pa November 12, 2013, dziko la Armenia linatulutsa m’ndende anthu onse a Mboni za Yehova omwe anamangidwa atakana kulowa usilikali chifukwa cha chikhulupiriro chawo. Vidiyoyi ikusonyeza zimene zinachitika pa mlanduwu mpaka pamene anthu a Mboniwa anatulutsidwa m’ndende.