NSANJA YA OLONDA November 2013

NKHANI YAPACHIKUTO

Zimene Zimapangitsa Anthu Ena Kuti Asamakonde Mulungu

Kodi mumaona kuti Mulungu sakhudzidwa ndi mavuto anu? Kodi Mulungu ndi wopanda chikondi? Werengani nkhaniyi kuti mudziwe chifukwa chake anthu ena amaganiza choncho.

NKHANI YAPACHIKUTO

Bodza Loyamba: Mulungu Alibe Dzina

Kodi anthu angalidziwedi dzina la Mulungu n’kumalitchula? N’chifukwa chiyani kudziwa dzinali n’kofunika?

NKHANI YAPACHIKUTO

Bodza Lachiwiri: Mulungu ndi Wosamvetsetseka

Chiphunzitso cha Utatu chimapangitsa kuti anthu asadziwe Mulungu komanso kumukonda. Kodi mungakonde munthu amene n’zosatheka kumudziwa bwino kapena amene simungamumvetsetse?

NKHANI YAPACHIKUTO

Bodza Lachitatu: Mulungu ndi Wankhanza

Ambiri amakhulupirira kuti Mulungu amalanga ochimwa kumoto kwamuyaya. Kodi Mulungu ndi wankhanza? Kodi n’chiyani chimachitikira munthu akamwalira?

NKHANI YAPACHIKUTO

Choonadi Chidzakumasulani

Kodi Yesu anatchula mfundo iti imene ingatithandize kuzindikira ngati ziphunzitso zachipembedzo zili zolondola kapena ayi?