NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA July 2018

M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira pa September 3-30, 2018.

Kodi Mumafuna Kukhala Wodziwika kwa Ndani?

Kodi tikuphunzira chiyani pa zimene Mulungu amachita posonyeza kuti amadziwa komanso kuyamikira atumiki ake okhulupirika?

Kodi Maso Anu Amayang’ana kwa Ndani?

Tingaphunzire mfundo yofunika kwambiri pa zimene Mose analakwitsa.

“Ndani Ali Kumbali ya Yehova?”

Nkhani za m’Baibulo zokhudza Kaini, Solomo, Mose ndi Aroni zimasonyeza kuti ndi nzeru kukhala kumbali ya Yehova.

Ndife Anthu a Yehova

Kodi tingathokoze bwanji Yehova chifukwa chotipatsa mwayi wokhala naye pa ubwenzi?