NSANJA YA MLONDA—YOPHUNZILA August 2018
Magazini ino ili na nkhani zophunzila wiki ya October 1-28, 2018.
Kodi Mudziŵa Bwino Zoona Zake?
Ni mfundo zitatu ziti za m’Baibo zimene zingatithandize kupenda mosamala zimene tamvela kuti tidziŵe ngati n’zoona?
Musamaweluze Poona Maonekedwe Akunja
Onani mbali zitatu zimene zionetsa kuti kuweluza ena poona maonekedwe awo akunja si cinthu canzelu.
MBILI YANGA
N’natsimikiza Mtima Kuti Sinidzabwelela M’mbuyo
Mvelani zocitika zimene m’bale Maxim Danyleyko wasangalala nazo m’zaka 68 zimene watumikila monga mmishonale.
Opatsa Mowoloŵa Manja Amakhala Acimwemwe
Kodi kukhala owolowa manja kumatithandiza bwanji kukhala acimwemwe?
Muziseŵenza na Yehova Tsiku Lililonse
Kodi tingaseŵenze na Yehova m’njila 5 ziti?
Kuleza mtima Kumatanthauza Kupilila Tili na Colinga
Phunzilani zimene kuleza mtima kumatanthauza, mmene tingakulitsile khalidweli, na mapindu amene tingapeze tikakhala oleza mtima
ZA M'NKHOKWE YATHU
Kufesa Mbewu za Ufumu ku Portugal
Ni mavuto anji amene alaliki a Ufumu oyambilila ku Portugal anakumana nawo?