NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA January 2019
“Usayang’ane Uku ndi Uku Mwamantha, Pakuti Ine Ndine Mulungu Wako”
Onani zifukwa zitatu zotithandiza kuti tizikhala odekha ngakhale pamene tikukumana ndi mavuto.
Tizitamanda Yehova Mumpingo
Kodi mumavutika kuyankha pamisonkhano? Nkhaniyi ingakuthandizeni kuzindikira vuto lanu komanso kudziwa zimene mmene mungathetsere vutolo.
Kodi Tingateteze Bwanji Mtima Wathu?
Kodi Satana amachita zotani pofuna kusokoneza mtima wathu, nanga tingauteteze bwanji?
Mwambo wa Chikumbutso Umasonyeza Makhalidwe a Mfumu Yakumwamba
Kodi mwambo wa Chikumbutso umasonyeza bwanji kuti Yesu ndi wachikondi, wodzichepetsa komanso wolimba mtima?
Makhalidwe Amene Amatichititsa Kupezeka Pamisonkhano
Kodi kudzichepetsa, chikondi komanso kulimba mtima zimatithandiza bwanji kuti tizipezeka pamisonkhano?