NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA February 2019
Pitirizani Kukhala ndi Mtima Wosagawanika
Kodi kukhala ndi mtima wosagawanika n’kutani nanga tingatani kuti tipitirize kukhala ndi khalidweli?
Yesetsani Kukhala Ofatsa Kuti Muzisangalatsa Yehova
Kodi Yesu ndi Mose anapereka chitsanzo chotani pa nkhani yokhala ofatsa? Kodi kukhala ofatsa n’kothandiza bwanji masiku ano?
Tizisonyeza Kuti Ndife Oyamikira
Kodi tingaphunzire chiyani kwa Yehova, Yesu ndi Msamaliya wakhate pa nkhani yosonyeza kuyamikira?
Aisiraeli Ankafunika Kusonyeza Chikondi ndi Chilungamo
Kodi Chilamulo cha Mose chimasonyeza chiyani pa mmene Yehova amaonera chikondi komanso chilungamo?