NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA October 2019

Tizitumikira Yehova Mwakhama Kumapeto kwa ‘Masiku Otsirizawa’

Kodi ndi zinthu ziti zimene zidzachitike kumapeto kwa “masiku otsiriza”? Ndipo kodi Yehova amafuna tizitani pamene tikuyembekezera zinthu zimenezi?

Tidzakhalebe Okhulupirika pa “Chisautso Chachikulu”

Kodi Yehova adzafuna kuti tidzatani pa nthawi ya “chisautso chachikulu”? Kodi tingakonzekere bwanji panopa kuti tidzakhalebe okhulupirika?

Kodi Yehova Adzakuthandizani Kuchita Chiyani?

Kale, Yehova anapatsa atumiki ake mtima wofuna kuchita zambiri komanso mphamvu zochitira zinthuzo. Kodi Yehova amatithandiza bwanji kuti tizimutumikira masiku ano?

Tizikhala Odzipereka kwa Yehova Yekha

Onani zinthu ziwiri zimene zingatithandize kudziwa ngati ndife odzipereka kwa Yehova yekha kapena ayi.