Danieli: Citsanzo Cokhala Wokhulupilika kwa Moyo Wonse

Danieli: Citsanzo Cokhala Wokhulupilika kwa Moyo Wonse—Gawo 1

Kodi Danieli adzakhalabe wokhulupilika kwa Mulungu wake Yehova, pamene ali kutali na banja la kwawo, komanso mzinda wa kwawo uli matongwe?

Danieli: Citsanzo Cokhala Wokhulupilika kwa Moyo Wonse—Gawo 2

Ufumu wamphamvu utenga ulamulilo. Danieli ayang’ananizana na adani atsopano. Cikhulupililo cake ciyesedwa kuposa ni kale lonse.