Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Zimene Achinyamata Anzanu Amanena

Onerani mavidiyo a achinyamata a m’mayiko osiyanasiyana akufotokoza mavuto amene amakumana nawo komanso zimene amachita pothana ndi mavutowo.

 

Ndingatani Ngati Anzanga Amandivutitsa?

Simungathe kuchititsa kuti anthu asamakuvutitseni, koma mungathe kusintha mmene mumawayankhira.

Zimene Achinyamata Amanena pa Nkhani Yochita Zinthu Mozengereza

Imvani zimene achinyamata anzanu akufotokoza pa za kuipa kochita zinthu mozengereza ndiponso ubwino wochita zinthu mosazengereza.

Kodi Ndili pa Ubwenzi ndi Yehova?

Kudziwa yankho la funsoli kungakuthandizeni kuthana ndi mavuto amene mukukumana nawo.

Zimene Achinyamata Amanena pa Nkhani ya Maonekedwe

N’chifukwa chiyani achinyamata ambiri zimawavuta kuti azisangalala ndi mmene amaonekera? N’chiyani chingawathandize pa nkhaniyi?

Ndingatani Ngati Anzanga Akundikakamiza Kuti Ndichite Zachiwerewere?

Pali mfundo zitatu za m’Baibulo zomwe zingakuthandizeni kukana mayesero.

Achinyamata Ena Akufotokoza Zokhudza Kukhulupirira Kuti Kuli Mulungu

M’vidiyo ya maminitsi atatuyi, achinyamata akufotokoza chifukwa chake amakhulupirira kuti kuli Mulungu.

Kodi N’zomveka Kukhulupirira Kuti Mulungu Alipo?

Onani achinyamata awiri amene anapeza mayankho a mafunso awo n’kulimbitsa chikhulupiriro chawo.

Kodi Baibulo Lingandithandize Bwanji?

Yankho la funso limeneli lingakuthandizeni kuti muzisangalala kwambiri pa moyo wanu.

Achinyamata Akukambirana Zokhudza Kuwerenga Baibulo

Kuwerenga sikophweka, koma kuwerenga Baibulo n’kothandiza kwambiri. Achinyamata anayi akufotokoza mmene kuwerenga Baibulo kwawathandizira.

Ndingatani Kuti Ndikonze Zomwe Ndinalakwitsa M’mbuyo?

Musaganize kuti kukonza zomwe munalakwitsa n’kovuta kwambiri.

Cameron Anapeza Moyo Wabwino Kwambiri

Kodi mukufuna kukhala munthu wosangalala? Mvetserani pamene Cameron akufotokoza zimene zinamuthandiza kuti akhale wosangalala atapita kumalo amene samaganizira kuti angafikeko.