NDANDANDA YA UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU April 2016
Zitsanzo za Ulaliki
Mfundo zothandiza pogawira Galamukani! ndi buku la Baibulo Limaphunzitsa Chiyani. Gwiritsani ntchito zitsanzozi kuti mukonze ulaliki wanuwanu.
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Tizilimbikitsa Anzathu Powayankhula Mokoma Mtima
M’malo momulimbikitsa anzake atatu a Yobu ankangomuonjezera ululu mwa kumuuza mawu osalimbikitsa komanso kumuimba milandu yabodza. (Yobu 16-20)
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Nkhani Zatsopano Zothandiza Poyamba Kukambirana ndi Anthu
Gwiritsani ntchito nkhani yatsopano yamutu wakuti “Kodi Baibulo Limanena Zotani?” poyamba kukambirana ndi anthu
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Yobu Sanalole Kuti Maganizo Olakwika Amusokoneze
Onani kusiyana kwa mabodza a Satana ndi mmene Yehova amationera. (Job 21-27)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Yobu Ndi Chitsanzo Chabwino pa Nkhani ya Kukhala ndi Mtima Wosagawanika
Yobu ankayesetsa kutsatira mfundo za Yehova za makhalidwe abwino ndipo anali wachilungamo. (Yobu 28-32)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Mnzako Weniweni Amakuuza Malangizo Othandiza
Muzikonda ena ngati mmene Elihu ankakondera Yobu. (Yobu 33-37)
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Ntchito Yoitanira Anthu Kumsonkhano Wachigawo
Zinthu zofunika kukumbukira pogawira timapepala toitanira anthu kumsonkhano wachigawo wa Mboni za Yehova. Yesererani chitsanzo cha ulaliki.
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Zofunika Kukumbukira Pamsonkhano Wachigawo
Ganizirani mmene mungasonyezere ena chikondi pamsonkhano.