Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

April 11-17

YOBU 21-27

April 11-17
  • Nyimbo Na. 83

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 129

  • Kodi Mungatani Kuti Anzanu Asiye Kukuvutitsani?: (15 min.) Nkhani yokambirana. Yambani ndi kuonetsa vidiyo ya pawebusaiti yathu ya jw.org/ny yakuti, Kodi Mungatani Kuti Anzanu Asiye Kukuvutitsani? (Pitani pamene palembedwa kuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ACHINYAMATA.) Kenako kambiranani mafunso otsatirawa: Kodi munthu angavutitsidwe pazifukwa ziti? Kodi munthu yemwe amavutitsidwa angakumane ndi mavuto ati? Kodi mungatani ngati anzanu amakuvutitsani kapenanso kuti asamakuvutitseni? Kodi mungauze ndani ngati wina akukuvutitsani? Pomaliza fotokozani mfundo za m’buku la Mayankho a Zimene Achinyamata Amadzifunsa, Buku Lachiwiri mutu 14.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: cl mutu 28 ndime 18-21 ndi bokosi patsamba 289 (30 min.)

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 23 ndi Pemphero