Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

April 18-24

YOBU 28-32

April 18-24
  • Nyimbo Na. 17 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: g16.2 12-13—Muuzeni nkhani imene mudzakambirane ulendo wotsatira. (Osapitirira 2 min.)

  • Ulendo Wobwereza: g16.2 12-13—Muuzeni nkhani imene mudzaphunzire ulendo wotsatira. (Osapitirira 4 min.)

  • Phunziro la Baibulo: bh 148 ndime 8-9 (Osapitirira 6 min.)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 115

  • Tingaphunzire Zambiri kwa Anthu Amene Anasonyeza Mtima Wosagawanika (1 Pet. 5:9): (15 min.) Nkhani yokambirana. Onetsani vidiyo ya mutu wakuti, Harold King Anakhalabe Wokhulupirika M’ndende (Vidiyo imeneyi ikupezeka pa jw.org pambali yakuti Zofalitsa Nkhani pa akaunti ya mpingo wanu.) Kenako kambiranani mafunso otsatirawa: Kodi n’chiyani chinathandiza M’bale King kuti asasiye kutumikira Yehova pamene anali m’ndende? Kodi kuimba nyimbo za Ufumu kungatithandize bwanji kupirira tikamakumana ndi mavuto? Kodi zimene M’bale King anachita zakulimbikitsani bwanji?

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: cl mutu 29 ndime 1-10 (30 min.)

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 81 ndi Pemphero