CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YOBU 28-32
Yobu Ndi Chitsanzo Chabwino pa Nkhani ya Kukhala ndi Mtima Wosagawanika
Yobu ankatsatira mfundo za makhalidwe abwino za Yehova ndi mtima wonse
Iye ankakonda kwambiri mkazi wake ndipo sanalole kuti maso ake aziyang’ananitsitsa akazi ena mowalakalaka
Yobu ndi chitsanzo chabwino pa nkhani ya kukhala bwino ndi ena
Anali wodzichepetsa, wachilungamo ndiponso wachifundo. Ankakonda anthu onse, olemera ndi osauka omwe
Yobu anali woolowa manja ndiponso sanali wodzikonda
Ankathandiza anthu ovutika