Mnzako Weniweni Amakuuza Malangizo Othandiza
Elihu atayamba kuyankhula, ananena malangizo abwino kwambiri kusiyana ndi amene ananena Elifazi, Bilidadi ndi Zofari. Ankachitanso zinthu mokoma mtima pa nthawi imene ankayankhula ndi Yobu. Zimene anachitazi zikusonyeza kuti anali mnzake weniweni wa Yobu amene anamuthandizadi. Ndipo ife tingachite bwino kumutsanzira.
MLANGIZI WABWINO AYENERA KUKHALA: |
ELIHU NDI CHITSANZO CHABWINO |
---|---|
|
|
|
|
|
|
|
|
|
|
|
|