Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

April 4-10

YOBU 16-20

April 4-10
  • Nyimbo Na. 79 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Tizilimbikitsa Anzathu Powayankhula Mokoma Mtima”: (10 min.)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Yobu 19:20 [Mawu am’munsi]—Kodi Yobu ankatanthauza chiyani pamene ananena kuti, “Ndapulumuka ndi khungu la mano anga”? (w06 3/15 14 ndime 13; it-2-E 977 ndime 1)

    • Yobu 19:26—Popeza kuti munthu sangathe kuona Yehova, kodi Yobu ankatanthauza chiyani ponena kuti “ndidzaona Mulungu”? (w94 11/15 19 ndime 17)

    • Kodi ndaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo ziti zimene ndaphunzira mlungu uno zimene ndingazigwiritse ntchito mu utumiki?

  • Kuwerenga Baibulo: Yobu 19:1-23 (Osapitirira 4 min.)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Kukonzekera Ulaliki wa Mwezi Uno: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onetsani mavidiyo a zitsanzo za ulaliki ndipo kenako kambiranani mfundo zikuluzikulu za m’mavidiyowo. Limbikitsani ofalitsa kuti akonze ulaliki wawowawo.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU