April 17-23
YEREMIYA 25-28
Nyimbo Na. 137 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Khalani Olimba Mtima Ngati Yeremiya”: (10 min.)
Yer. 26:2-6—Yehova anatuma Yeremiya kuti alengeze uthenga wochenjeza anthu (w09 12/1 24 ¶6)
Yer. 26:8, 9, 12, 13—Yeremiya sanaope anthu amene ankadana naye (jr 21 ¶13)
Yer. 26:16, 24—Yehova anateteza mneneri wake wolimba mtimayu (w09 12/1 25 ¶1)
Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)
Yer. 27:2, 3—Kodi n’chifukwa chiyani amithenga ochokera m’mitundu yosiyanasiyana anabwera ku Yerusalemu, nanga n’chifukwa chiyani Yeremiya anawapangira magoli? (jr 27 ¶21)
Yer. 28:11—Kodi Yeremiya anachita bwanji zinthu mwanzeru pamene Hananiya ankamutsutsa, ndipo tikuphunzira chiyani pa chitsanzo chakechi? (jr 187-188 ¶11-12)
Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Yer. 27:12-22
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) T-36—Muuzeni nkhani imene mudzakambirane ulendo wotsatira.
Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) T-36—Muuzeni nkhani imene mudzakambirane ulendo wotsatira.
Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) lv 7 ¶4-5—Sonyezani mmene tingafikire pamtima wophunzira wathu.
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Nyimbo Na. 17
“Nyimbo za Ufumu Zimatithandiza Kuti Tikhale Olimba Mtima”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onetsani vidiyo yakuti Nyimbo Imene Inalimbikitsa Akaidi.
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) ia mutu 22 ¶1-13
Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)
Nyimbo Na. 26 ndi Pemphero