Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

April 17-23

YEREMIYA 25-28

April 17-23

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Khalani Olimba Mtima Ngati Yeremiya”: (10 min.)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Yer. 27:2, 3​—Kodi n’chifukwa chiyani amithenga ochokera m’mitundu yosiyanasiyana anabwera ku Yerusalemu, nanga n’chifukwa chiyani Yeremiya anawapangira magoli? (jr 27 ¶21)

    • Yer. 28:11​—Kodi Yeremiya anachita bwanji zinthu mwanzeru pamene Hananiya ankamutsutsa, ndipo tikuphunzira chiyani pa chitsanzo chakechi? (jr 187-188 ¶11-12)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Yer. 27:12-22

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) T-36​—Muuzeni nkhani imene mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) T-36​—Muuzeni nkhani imene mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) lv 7 ¶4-5​—Sonyezani mmene tingafikire pamtima wophunzira wathu.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU