NDANDANDA YA UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU April 2019
Zimene Tinganene
Zitsanzo za ulaliki zofotokoza za imfa ya Yesu Khristu.
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Kusakhala Pabanja ndi Mphatso
Kodi Mkhristu angatani kuti azigwiritsa ntchito nthawi yake mwanzeru pamene sali pabanja?
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Yehova ndi Wokhulupirika
Tikakumana ndi mayesero, Yehova amatipatsa zinthu zofunikira kuti tithe kupilira.
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Kodi Muchikonzekera Bwanji Chikumbutso?
Tonsefe tiyenera kukonzekeretsa mtima wathu. Koma kodi tingachite bwanji zimenezi?
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Mulungu Adzakhala “Zinthu Zonse kwa Aliyense”
Anthu amene ndi okhulupirika kwa Yehova adzakhala ndi tsogolo labwino kwambiri.
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Yehova ndi “Mulungu Amene Amatitonthoza M’njira Iliyonse”
Njira imodzi imene Yehova amagwiritsa ntchito potitonthoza ndi kugwiritsira ntchito abale ndi alongo athu mumpingo.
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Dziperekeni Kuti Yehova Akuphunzitseni
Yehova, yemwe ndi Mlangizi wathu wamkulu, amatipatsa maphunziro apamwamba kwambiri