Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

April 27–May 3

GENESIS 34-35

April 27–May 3

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Kuopsa Kocheza ndi Anthu a Makhalidwe Oipa”: (10 min.)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Ge 35:8​—Kodi Debora anali ndani, nanga tingaphunzire chiyani kwa iye? (it-1 600 ¶4)

    • Ge 35:22-26​—Kodi tikudziwa bwanji kuti si nthawi zonse pamene mwana woyamba kubadwa ankayenera kukhala mumzere wa makolo a Mesiya? (w17.12 14)

    • Kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Ge 34:1-19 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

MOYO WATHU WACHIKHRISTU