Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

August 22-28

MASALIMO 106-109

August 22-28
  • Nyimbo Na. 2 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) ll 6—Siyani funso loti mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) ll 7—Siyani funso loti mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) bh 178-179 ndime 14-16—Muthandizeni wophunzirayo kuona mmene angagwiritsire ntchito mfundo za m’ndimezi.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 94

  • Yehova Adzatisamalira (Sal. 107:9): (15 min.) Nkhani yokambirana. Yambani ndi kuonetsa vidiyo yakuti, Yehova Adzatisamalira. (Pitani pamene alemba kuti MAVIDIYO ENA > BANJA.) Pemphani omvera kuti afotokoze zimene tikuphunzirapo.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) ia mutu 5 ndime 1-13.

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 149 ndi Pemphero