NDANDANDA YA UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU December 2018
Zimene Tinganene
Zitsanzo za zimene tinganene zokhudza cholinga cha mulungu polenga anthu komanso zimene akutilonjeza m’tsogolomu.
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Munthu Amene Ankazunza Akhristu Anakhala Mkhristu Wakhama
Ngati mukuphunzira Baibulo koma simunabatizidwe, kodi mungakonde kutsanzira Saulo n’kuyamba kuchita mogwirizana ndi zimene mwaphunzira?
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Baranaba ndi Paulo Ankathandiza Anthu Kukhala Ophunzira M’madera Akutali Kwambiri
Baranaba ndi Paulo anagwira ntchito mwakhama pothandiza anthu ofatsa kuti akhale Akhristu.
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Muzithandiza Anthu Amene Ali ndi “Maganizo Abwino” Kuti Akhale Ophunzira
Kodi timagwira ntchito bwanji ndi Yehova tikamathandiza anthu kuti akhale ophunzira?
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Anasankha Zochita Pogwiritsa Ntchito Mawu a Mulungu
Kodi tikuphunzira chiyani pa nkhani yokhudza mmene nkhani yamdulidwe inathetsedwera?
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Tizitamanda Yehova Mosangalala Poimba Nyimbo
Kodi timapindula bwanji tikamaimba nyimbo za Ufumu?
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Muzitsanzira Mtumwi Paulo pa Nkhani Yolalikira Komanso Kuphunzitsa
Kodi tingatsanzire bwanji Paulo tikamalalikira?
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Mukhale Tcheru ndi Kuyang’anira Gulu Lonse la Nkhosa”
Akulu amadyetsa, kuteteza, komanso kusamalira nkhosa, chifukwa amakumbukira kuti nkhosa iliyonse inagulidwa ndi magazi a mtengo wapatali a Yesu.