Muzitsanzira Mtumwi Paulo pa Nkhani Yolalikira Komanso Kuphunzitsa
Kodi tingatsanzire bwanji Paulo?
-
Tizigwiritsa ntchito Malemba tikamakambirana ndi anthu komanso kumasintha ulaliki wathu kuti ugwirizane ndi anthu amene takumana nawo
-
Tizilalikira kumalo komanso pa nthawi imene tingakumane ndi anthu ambiri
-
Tizichita zinthu mwaluso poyesetsa kudziwa zimene anthu amakhulupirira n’kugwiritsa ntchito zimenezo poyamba kukambirana nawo