Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MACHITIDWE 19-20

“Mukhale Tcheru ndi Kuyang’anira Gulu Lonse la Nkhosa”

“Mukhale Tcheru ndi Kuyang’anira Gulu Lonse la Nkhosa”

20:28, 31, 35

Akulu amadyetsa, kuteteza ndi kusamalira nkhosa chifukwa amadziwa kuti nkhosazo zinagulidwa ndi magazi a mtengo wapatali a Yesu. Abale ndi alongo amayamikira kwambiri akulu omwe ali ngati Paulo, amene amadzipereka posamalira nkhosa.