December 9-15
CHIVUMBULUTSO 10-12
Nyimbo Na. 26 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“‘Mboni Ziwiri’ Zinaphedwa Koma Zinakhalanso ndi Moyo”: (10 min.)
Chiv. 11:3—“Mboni ziwiri” zinanenera kwa masiku 1,260 (w14 11/15 30)
Chiv. 11:7—Mbonizi zinaphedwa ndi “chilombo”
Chiv. 11:11—“Mboni ziwiri” zija zinakhalanso ndi moyo patadutsa “masiku atatu ndi hafu”
Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)
Chiv. 10:9, 10—Kodi uthenga umene Yohane analandira unakhala bwanji wowawa komanso wotsekemera? (it-2 880-881)
Chiv. 12:1-5—Kodi mavesi amenewa anakwaniritsidwa bwanji? (it-2 187 ¶7-9)
Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Chiv. 10:1-11 (th phunziro 10)
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.
Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo woyamba. (th phunziro 6)
Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo woyamba. Sonyezani mmene mungalalikirire mwamwayi malinga ndi zimene zimakonda kuchitika m’dera lanu. (th phunziro 3)
Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo woyamba. Kenako mugawireni chimodzi mwa Zinthu Zophunzitsira. (th phunziro 9)
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
“Dziko ‘Linameza Mtsinje’”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Abale a ku Korea Atulutsidwa M’ndende.
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 63
Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)
Nyimbo Na. 103 ndi Pemphero