February 15-21
NEHEMIYA 9-11
Nyimbo Na. 84 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Anthu Okhulupirika Amatsatira Malangizo a Gulu la Yehova”: (10 min.)
Neh. 10:28-30—Anamvera zoti asakwatirane ndi “anthu a m’mayikowo” (w98 10/15 21 ndime 11)
Neh. 10:32-39—Iwo anatsimikiza kuti azithandiza pa kulambira koona (w98 10/15 21 ndime 11-12)
Neh. 11:1, 2—Anamvera ndi mtima wonse malangizo a gulu la Yehova (w06 2/1 11 ndime 6; w98 10/15 22 ndime 13)
Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)
Neh. 9:19-21—Kodi Yehova anasonyeza bwanji kuti amapereka kwa anthu ake zinthu zofunika? (w13 9/15 9 ndime 9-10)
Neh. 9:6-38—Kodi Alevi anapereka chitsanzo chotani pa nkhani yopemphera? (w13 10/15 22-23 ndime 6-7)
Kodi ndaphunzira chiyani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kodi ndi mfundo ziti zimene ndaphunzira mlungu uno zimene ndingazigwiritse ntchito mu utumiki?
Kuwerenga Baibulo: Neh. 11:15-36 (Osapitirira 4 min.)
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Gawirani Galamukani! yatsopano pogwiritsa ntchito mutu wakuti “Mfundo Zothandiza Mabanja—Kodi Mungatani Kuti Mukhale ndi Anzanu Apamtima?” Muuzeni zimene mudzakambirane mukadzabweranso.
Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Chitani chitsanzo chosonyeza ulendo wobwereza kwa munthu amene anasangalala ndi mutu wakuti “Mfundo Zothandiza Mabanja—Kodi Mungatani Kuti Mukhale ndi Anzanu Apamtima?” Muuzeni nkhani yomwe mudzaphunzire mukadzabweranso.
Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) Chitani chitsanzo chosonyeza mukuphunzira ndi munthu. (bh 32-33 ndime 13-14)
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Nyimbo Na. 19
“Moyo Wabwino Kwambiri”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Yambani ndi kuonetsa vidiyo. Kenako kambiranani mafunso. Funsani wofalitsa mmodzi yemwe ali pabanja kapena amene sali pabanja yemwe wachita zambiri potumikira Yehova asanalowe m’banja. (1 Akor. 7:35) Kodi anadalitsidwa bwanji?
Phunziro la Baibulo la Mpingo: cl mutu 26 ndime 1-9 (30 min.)
Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)
Nyimbo Na. 76 ndi Pemphero