Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

February 15-21

NEHEMIYA 9-11

February 15-21
  • Nyimbo Na. 84 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 19

  • Moyo Wabwino Kwambiri”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Yambani ndi kuonetsa vidiyo. Kenako kambiranani mafunso. Funsani wofalitsa mmodzi yemwe ali pabanja kapena amene sali pabanja yemwe wachita zambiri potumikira Yehova asanalowe m’banja. (1 Akor. 7:35) Kodi anadalitsidwa bwanji?

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: cl mutu 26 ndime 1-9 (30 min.)

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 76 ndi Pemphero