Nehemiya Anali Woyang’anira Wabwino
Tishiri 455 B.C.E.
-
N’kutheka kuti panthawiyi m’pamene Nehemiya anasonkhanitsa anthu kuti alambire Yehova
-
Anthu anasangalala kwambiri
-
Anthu amene anali mitu ya mabanja anasonkhana kuti aone zimene angachite kuti azitsatira kwambiri Chilamulo cha Mulungu
-
Anthu anakonzekera kuchita Chikondwerero cha Misasa