February 19-25
MATEYU 16-17
Nyimbo Na. 45 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Kodi Mumayendera Maganizo a Ndani?”: (10 min.)
Mat. 16:21, 22—Petulo analola kuti kutengeka maganizo kuzilamulira kaganizidwe kake (w07 2/15 16 ¶17)
Mat. 16:23—Petulo anasiya kuyendera maganizo a Mulungu (w15 5/15 13 ¶16-17)
Mat. 16:24—Akhristu ayenera kumayendera maganizo a Mulungu (w06 4/1 23 ¶9)
Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)
Mat. 16:18—Kodi ndi ndani amene anali thanthwe lomwe Yesu anamangapo mpingo wachikhristu? (“Iwe ndiwe Petulo, ndipo pathanthwe ili” “mpingo” mfundo zimene ndikuphunzira pa Mat. 16:18, nwtsty)
Mat. 16:19—Kodi “makiyi a Ufumu wakumwamba” amene Yesu anapatsa Petulo anali chiyani? (“makiyi a Ufumu wakumwamba” mfundo zimene ndikuphunzira pa Mat. 16:19, nwtsty)
Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Mat. 16:1-20
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo woyamba. Sonyezani mmene mungayankhire pa nkhani inayake yomwe anthu a m’gawo lanu amatsutsa kawirikawiri.
Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha zimene tinganene.
Vidiyo ya Ulendo Wobwereza Wachiwiri: (5 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
“Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Muzigwiritsa Ntchito Mafunso Mwaluso”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Muzigwira Ntchito Imene Yesu Anagwira—Muziphunzitsa.
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 14 ¶8-14 komanso bokosi patsamba 150
Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)
Nyimbo Na. 134 ndi Pemphero