Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

February 5-​11

MATEYU 12-13

February 5-​11

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Fanizo la Tirigu ndi Namsongole”: (10 min.)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Mat. 12:20​—Kodi tingatsanzire bwanji khalidwe la Yesu lochitira ena chifundo? (“nyale yofuka” mfundo zimene ndikuphunzira pa Mat. 12:20, nwtsty)

    • Mat. 13:25​—Kodi zinkachitikadi kuti munthu ankafesa namsongole m’munda umene mnzake wafesamo tirigu? (w16.10 32)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Mat. 12:1-21

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha zimene tinganene.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) bhs 22-23 ¶10-12

MOYO WATHU WACHIKHRISTU