February 5-11
MATEYU 12-13
Nyimbo Na. 27 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Fanizo la Tirigu ndi Namsongole”: (10 min.)
Mat. 13:24-26—Munthu anafesa mbewu zabwino m’munda mwake, koma mdani wake anabwera n’kudzafesamo namsongole (w13 7/15 9-10 ¶2-3)
Mat. 13:27-29—Tirigu ndi namsongole zinakulira pamodzi mpaka nthawi yokolola (w13 7/15 10 ¶4)
Mat. 13:30—Nthawi yokolola itafika, okolola anasonkhanitsa namsongole kenako anasonkhanitsa tirigu (w13 7/15 12 ¶10-12)
Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)
Mat. 12:20—Kodi tingatsanzire bwanji khalidwe la Yesu lochitira ena chifundo? (“nyale yofuka” mfundo zimene ndikuphunzira pa Mat. 12:20, nwtsty)
Mat. 13:25—Kodi zinkachitikadi kuti munthu ankafesa namsongole m’munda umene mnzake wafesamo tirigu? (w16.10 32)
Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Mat. 12:1-21
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.
Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha zimene tinganene.
Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) bhs 22-23 ¶10-12
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Zofunika Pampingo: (5 min.)
“Mfundo Zimene Tingaphunzire Kuchokera M’mafanizo Onena za Ufumu”: (10 min.) Nkhani yokambirana. Kambiranani mmene mafanizo amenewa angatithandizire kuti tizichita khama polalikira.
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 13 ¶33-34 ndi bokosi patsamba “145 komanso tsamba 146-147
Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)
Nyimbo Na. 10 ndi Pemphero