Kodi ‘Mukudikira Mwachidwi’?
-
“Chilengedwe”: anthu amene akuyembekezera kudzakhala padziko lapansi
-
‘Ulemelero wa ana a Mulungu udzaonekera’: pamene odzozedwa adzathandiza Yesu kuwononga dziko loipa la Satanali
-
“Maziko a chiyembekezo”: zimene Yehova akulonjeza kuti adzatipulumutsa kudzera mu imfa komanso kuukitsidwa kwa Yesu
-
‘Kumasulidwa ku ukapolo wa kuvunda’: anthu adzayamba kumasulidwa pang’onopang’ono kuchokera ku mavuto amene amabwera chifukwa cha uchimo ndi imfa