Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

February 25–March 3

AROMA 9-11

February 25–March 3

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Fanizo la Mtengo wa Maolivi”: (10 min.)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Aroma 9:21-23​—N’chifukwa chiyani tiyenera kulola kuumbidwa ndi Yehova yemwe ndi Woumba Mbiya Wamkulu? (w13 6/15 25 ¶5)

    • Aroma 10:2​—N’chifukwa chiyani tiyenera kudziwa Mulungu molondola kuti tizimulambira movomerezeka? (it-1 1260 ¶2)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Aroma 10:1-15 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

MOYO WATHU WACHIKHRISTU