February 25–March 3
AROMA 9-11
Nyimbo Na. 25 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Fanizo la Mtengo wa Maolivi”: (10 min.)
Aroma 11:16—Mtengo wa Maolivi umaimira kukwaniritsidwa kwa cholinga cha Mulungu chokhudza pangano la Abulahamu (w11 5/15 23 ¶13)
Aroma 11:17, 20, 21—Odzozedwa omwe analumikizidwa kumtengo wophiphiritsa wa maolivi ayenera kupitiriza kukhala ndi chikhulupiriro (w11 5/15 24 ¶15)
Aroma 11:25, 26—Chiwerengero chokwanira cha Aisiraeli auzimu ‘chidzapulumuka’ (w11 5/15 25 ¶19)
Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)
Aroma 9:21-23—N’chifukwa chiyani tiyenera kulola kuumbidwa ndi Yehova yemwe ndi Woumba Mbiya Wamkulu? (w13 6/15 25 ¶5)
Aroma 10:2—N’chifukwa chiyani tiyenera kudziwa Mulungu molondola kuti tizimulambira movomerezeka? (it-1 1260 ¶2)
Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Aroma 10:1-15 (th phunziro 10)
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Vidiyo ya Ulendo Wobwereza Wachiwiri: (5 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.
Ulendo Wobwereza Wachiwiri: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza wachiwiri. (th phunziro 6)
Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 5 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza wachiwiri ndipo kenako yambitsani phunziro la Baibulo pogwiritsa ntchito buku la Zimene Baibulo Limaphunzitsa. (th phunziro 9)
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
“Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Kusiya Kuphunzira ndi Munthu Yemwe Sakupita Patsogolo”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo.
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 27
Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)
Nyimbo Na. 57 ndi Pemphero