CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AROMA 1-3 Pitirizani Kuphunzitsa Chikumbumtima Chanu YAMBANI Pitirizani Kuphunzitsa Chikumbumtima Chanu 2:14, 15 Chikumbumtima chathu chingatithandize kusankha bwino zochita ngati . . . timachiphunzitsa pogwiritsa ntchito mfundo za m’Baibulo timachimvera chikamatikumbutsa mfundozo timapempha mzimu woyera kuti utithandize kulimbana ndi matupi athu ochimwawa.—Aroma 9:1 Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena Pitirizani Kuphunzitsa Chikumbumtima Chanu NDANDANDA YA UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU Pitirizani Kuphunzitsa Chikumbumtima Chanu Chichewa Pitirizani Kuphunzitsa Chikumbumtima Chanu https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/202019043/univ/art/202019043_univ_sqr_xl.jpg