February 5-11
SALIMO 1-4
Nyimbo Na. 150 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)
1. Khalani ku Mbali ya Ufumu wa Mulungu
(10 min.)
[Onerani VIDIYO ya Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Masalimo.]
Maboma a anthu adzipanga kukhala adani a Mulungu (Sl 2:2; w21.09 15 ¶8)
Yehova akupereka mwayi kwa anthu onse kuti asankhe kukhala ku mbali ya Ufumu wake (Sl 2:10-12)
DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndine wotsimikiza mtima kusatenga nawo mbali pa zochitika za ndale za m’dzikoli, ngakhale zitaoneka kuti kuchita zimenezi kukhoza kundibweretsera mavuto?’—w16.04 29 ¶11.
2. Mfundo Zothandiza
(10 min.)
Sl 1:4—Kodi anthu oipa amafanana bwanji ndi “mankhusu amene amauluzika ndi mphepo”? (it-1 425)
Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
3. Kuwerenga Baibulo
(4 min.) Sl 3:1–4:8 (th phunziro 12)
4. Kukambirana Mwachibadwa—Zomwe Filipo Anachita
(7 min.) Nkhani yokambirana. Onerani VIDIYO, kenako kambiranani lmd phunziro 2 mfundo 1-2.
5. Kukambirana Mwachibadwa—Zomwe Mungachite Potsanzira Filipo
(8 min.) Nkhani yokambirana kuchokera mu kabuku ka lmd phunziro 2 mfundo 3-5 ndi “Onaninso Malemba Awa.”
Nyimbo Na. 32
6. Zofunika Pampingo
(15 min.)
7. Phunziro la Baibulo la Mpingo
(30 min.) bt mutu 5 ¶9-15, bokosi patsamba 41