Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

January 1-7

YOBU 32-33

January 1-7

Nyimbo Na. 102 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Elihu akumvetsera mwatcheru pamene Yobu akufotokoza mavuto ake

1. Muzilimbikitsa Amene Akulimbana ndi Nkhawa

(10 min.)

Mukamachita zinthu ndi ena muziwaona kuti ndi anzanu (Yob 33:1; it-1 710)

Muzikhala achifundo ndipo musamawaweruze (Yob 33:6, 7; w14 6/15 25 ¶8-10)

Musanalankhule, muzimvetsera n’kuganizira ngati mmene anachitira Elihu (Yob 33:8-12, 17; w20.03 23 ¶17-18; Onani chithunzi chapachikuto)

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Yob 33:25—Kodi lembali likutithandiza bwanji kuti pamene tikukalamba tisamadere nkhawa za mmene tikuonekera? (w13 1/15 19 ¶10)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Kuchita Chidwi ndi Anthu—Zomwe Yesu Anachita

(7 min.) Nkhani yokambirana. Onerani VIDIYO, kenako kambiranani kabuku ka lmd phunziro 1 mfundo 1-2.

5. Kuchita Chidwi ndi Anthu—Zomwe Mungachite Potsanzira Yesu

(8 min.) Nkhani yokambirana kuchokera mu kabuku ka lmd phunziro 1 mfundo 3-5 ndi “Onaninso Malemba Awa.”

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 116

6. Zofunika Pampingo

(15 min.)

7. Phunziro la Baibulo la Mpingo

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 54 ndi Pemphero