Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

January 13-19

MASALIMO 135-137

January 13-19

Nyimbo Na. 2 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. “Ambuye Wathu Ndi Wamkulu Kuposa Milungu Ina Yonse”

(10 min.)

Yehova wasonyeza kuti iye ndi amene amatsogolera chilengedwe chonse (Sl 135:5, 6; it-2 661 ¶4-5)

Amateteza anthu ake (Eks 14:29-31; Sl 135:14)

Amakhala nafe tikafooka (Sl 136:23; w21.11 6 ¶16)

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Sl 135:1, 5—N’chifukwa chiyani mawu akuti “Ya” nthawi zambiri amagwiritsidwa ntchito m’Baibulo? (it-1 1248)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Ulendo Woyamba

(3 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Uzanani kumene mumakhala komanso patsanani manambala a foni ndi munthu amene wasonyeza chidwi. (lmd phunziro 2 mfundo 4)

5. Ulendo Wobwereza

(4 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Muitanireni ku misonkhano yathu. (lmd phunziro 9 mfundo 4)

6. Kufotokoza Zimene Mumakhulupirira

(5 min.) Chitsanzo. ijwfq 7—Mutu: Kodi a Mboni za Yehova Ndi Akhristu? (th phunziro 12)

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 10

7. Zofunika Pampingo

(15 min.)

8. Phunziro la Baibulo la Mpingo

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 90 ndi Pemphero