NDANDANDA YA UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU July 2018
Zimene Tinganene
Zimene tinganene zokhudza mfundo za m’Baibulo zomwe zingathandize kuti mabanja azikhala osangalala.
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Muzikhala Owolowa Manja
Munthu wowolowa manja amasangalala akamagwiritsa ntchito zinthu zake pothandiza komanso kulimbikitsa ena.
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Kodi Chofunika N’chiyani Kuti Munthu Akhale Wotsatira wa Yesu?
Kodi tiyenera kumaganizira kwambiri chiyani ngati tayamba kusokonezedwa ndi zinthu zakumbuyo zimene tinasiya?
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Fanizo la Msamariya Wachifundo
Otsatira a Yesu ayenera kuchita zonse zomwe angathe kuti azikonda ena, ngakhale omwe amasiyana nawo m’zinthu zambiri.
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
N’chifukwa Chiyani Sitiyenera Kulowerera Ndale? (Mika 4:2)
Potsanzira Mulungu wathu yemwe ndi wopanda tsankho, tiyenera ‘kuchitira onse zabwino.’
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Ndinu Ofunika Kwambiri Kuposa Mpheta Zambiri”
Kodi tingatengere bwanji chitsanzo cha Yehova pa nkhani yoganizira anthu omwe akuzunzidwa?
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Fanizo la Mwana Wolowerera
Kodi tikuphunzira chiyani mu fanizo la Yesu la mwana wolowerera pa nkhani ya nzeru, kudzichepetsa komanso kudalira Yehova?