Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

July 23-29

Luka 12-13

July 23-29
  • Nyimbo Na. 4 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Ndinu Ofunika Kwambiri Kuposa Mpheta Zambiri”: (10 min.)

    • Luka 12:6​—Yehova samaiwala ngakhale mbalame zing’onozing’ono (“mpheta” mfundo zimene ndikuphunzira pa Luka 12:6, nwtsty)

    • Luka 12:7​—Zimene Yehova amadziwa zokhudza anthufe, zimasonyeza kuti amatiganizira kwambiri (“ngakhale tsitsi lonse la m’mutu mwanu analiwerenga” mfundo zimene ndikuphunzira pa Luka 12:7, nwtsty)

    • Luka 12:7​—Yehova amaona kuti munthu aliyense ndi wofunika (cl 241 ¶4-5)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Luka 13:24​—Kodi malangizo a Yesuwa akutanthauza chiyani? (“Yesetsani mwamphamvu” mfundo zimene ndikuphunzira pa Luka 13:24, nwtsty)

    • Luka 13:33​—N’chifukwa chiyani Yesu ananena mawu amenewa? (“n’kosayenera” mfundo zimene ndikuphunzira pa Luka 13:33, nwtsty)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Luka 12:22-40

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Wobwereza Wachiwiri: (Osapitirira 3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha zimene tinganene. Kenako muitanireni kumisonkhano yathu.

  • Ulendo Wobwereza Wachitatu: (Osapitirira 3 min.) Sankhani lemba lililonse ndipo gawirani buku kapena kabuku kamene timagwiritsa ntchito pophunzira ndi anthu.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) lv 185 ¶4-5

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 116

  • Tisawaiwale Ngakhale Amakhala Kwaokha: (15 min.) Onerani vidiyoyi. Kenako kambiranani mafunso otsatirawa:

    • Kodi ndi mavuto otani omwe ofalitsa atatu a m’vidiyoyi anakumana nawo?

    • Kodi Yehova anasonyeza bwanji kuti sanawaiwale?

    • Kodi ofalitsawa amachita chiyani kuti apitirizebe kutumikira Yehova ngakhale akukumana ndi mavuto, nanga zimenezi zalimbikitsa bwanji ena?

    • Kodi tingasonyeze bwanji kuti timakonda achikulire komanso ena omwe akudwala mumpingo wathu?

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 22 ¶1-7

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 5 ndi Pemphero