August 14-20
NEHEMIYA 8-9
Nyimbo Na. 110 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (1 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Chimwemwe Chimene Yehova Amapereka Ndicho Malo Anu Achitetezo”: (10 min.)
Mfundo Zothandiza: (10 min.)
Kuwerenga Baibulo: (4 min.) Ne 8:1-12 (th phunziro 10)
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Ulendo Woyamba: (3 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo woyamba. Mugawireni chimodzi mwa Zinthu Zophunzitsira. (th phunziro 13)
Ulendo Wobwereza: (4 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo wobwereza. Muitanireni ku misonkhano yathu, ndipo yerekezerani kumuonetsa vidiyo yakuti Kodi pa Nyumba ya Ufumu Pamachitika Zotani? kenako kambiranani naye mfundo za muvidiyoyi. (th phunziro 11)
Phunziro la Baibulo: (5 min.) lff phunziro 11 mfundo 5 komanso Zimene Ena Amanena (th phunziro 8)
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
“Zochita Zanu Zingathandize Banja Lanu Kukhala Losangalala”: (15 min.) Nkhani yokambirana komanso vidiyo.
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lff phunziro 54
Mawu Omaliza (3 min.)
Nyimbo Na. 123 ndi Pemphero